Chichewa
stringlengths 10
500
| sentiment
stringclasses 2
values | __index_level_0__
int64 0
835k
|
---|---|---|
Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?" | Negative | 0 |
Anthu atatu onsewa anasintha chonchi chifukwa choti ankafuna kutsanzira Khristu. | Negative | 1 |
"Ndipo iye pamodzi ndi makamu ake ankhondo adadzitukumula pa dziko popanda chilungamo ndipo ankaganiza kuti iwo sadzabwelere kwa Ife. | Negative | 2 |
njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)! | Positive | 3 |
"Ndipo opani Moto umene wakonzedwa kwa (anthu) osakhulupirira. | Negative | 4 |
"Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m'mphepete mwa nyanja; (anthu am'mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m'malo mwake azichita mapemphero okha). | Negative | 5 |
Amapereka moyo ndikupereka imfa, Mbuye wanu ndi Mbuye wa makolo anu oyamba. | Positive | 6 |
"Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m'dziko (la Iguputo); amakhala m'menemo paliponse pamene wafuna. | Positive | 7 |
"Ndipo munthu (wokanira) amanena: "Kodi ndikadzafa nzoonadi kuti Ndidzatulutsidwa (m'manda) nkukhala wamoyo?" | Negative | 8 |
Iye anayenda nane mwamtendere ndi molungama mtima, ndipo anabweza anthu ambiri mʼnjira zawo zauchimo. | Positive | 9 |
N'zimene zinawasonkhezera kukwaniritsa zimene anachita." | Positive | 10 |
Kodi Qur'an sinadzudzule ma Arabu achikunja chifukwa | Negative | 11 |
Ngakhale kuti kukhalapo kwake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu n'kosaoneka, umboni wake ukuoneka chifukwa cha kukwaniritsidwa kwa maulosi. | Negative | 12 |
Ndipo A'adi adaonongedwa ndi chimphepo | Positive | 13 |
Ndipo iye adaitana Mbuye wake kuti: "Awa ndithu ndi anthu oipa." | Negative | 14 |
""Ndithu Allah ndiye Mbuye wanga ndi Mbuye wanunso; choncho mupembedzeni; imeneyi ndiyo njira yolunjika." | Positive | 15 |
"Ndipo kachisanu (alumbire) kuti matembelero a Allah akhale pa iye ngati (iye) ali m'modzi mwa onama. | Negative | 16 |
(Zikadzachitika zimenezi) mzimu Uliwonse udzadziwa zimene Wabweretsa (zabwino ndi zoipa). | Positive | 17 |
Kuti tithawe kuchoka mnyanja yamoto, kulibe njira ina iliyonse koma kuti maina athu alembedwe mu Buku la Moyo. | Negative | 18 |
ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena. | Positive | 19 |
"Ndipo ndithu tidasiya chizindikiro mmenemo choonekera kwa anthu anzeru. | Positive | 20 |
Atumize Mzimu Wanu, ndipo iwo adzakhala analenga. | Positive | 21 |
"Kodi saona momwe Allah ayambitsira zolengedwa, kenako nkuzibwerezanso? | Negative | 22 |
"Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere). | Negative | 23 |
"Ndipo ngati utawafunsa: "Ndani adawalenga?" | Negative | 24 |
"Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu. | Positive | 25 |
"M'menemo ndi momwe tikulongosolera mokwanira zivumbulutso kuti mwina iwo angabwelere (kwa Allah). | Positive | 26 |
(Komanso) ndinasonkhanitsa anthu onse (amene ankakhala m'mizindayo) ndipo ndinawalamula kuti abwerere kumizinda yawo." | Positive | 27 |
Ndipo iwo adzakhala ndi moyo m'dziko lawo, limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo. | Positive | 28 |
Koma amene angafune (zina) Kusiya zimenezi iwowo ndiwo Olumpha malire. | Positive | 29 |
Ndithu m'zimenezo muli malingaliro kwa kapolo aliyense wotembenukira (kwa Allah). | Positive | 30 |
""Ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu." | Negative | 31 |
Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m'menemo muyaya. | Positive | 32 |
" (Zikadzachitika zimenezi) mzimu uliwonse udzadziwa zimene wabweretsa (zabwino ndi zoipa). | Positive | 33 |
Ndithudi, yemwe mudzamulowetse ku Moto ndiye kuti mwamuyalutsa, ndipo sipadzakhala athandizi kwa ochita zoipa." | Negative | 34 |
"Ndipo angelo awiriwa anadza ku Sodomu madzulo, pamene Loti adakhala pachipata cha Sodomu. | Negative | 35 |
Komanso tikulimbikitsidwa ndi mawu akuti: 'Omwe aopa Mulungu adzapeza bwino.' | Positive | 36 |
"Kwa yemwe mwa inu akufuna kuyenda mu njira yoongoka. | Positive | 37 |
Ndipo munthu adati kwa ena, | Positive | 38 |
Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha." | Negative | 39 |
Qur'an inabvumbulutsidwa Mmwezi wa Ramadhan, choncho Allah anaupanga mwezi wa Ramadhan kukhala wabwino kuposa myezi yonse. | Positive | 40 |
"Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha, | Negative | 41 |
Thangwe nsiku za wanthu wangu, zin'dzakhala ninga nsiku za muti, ndipo omwe ndawasankhulawo, wan'dzapfatsa na mabasa yakuphatidwa na manja yawo.' | Positive | 42 |
Ndipo opani Allah, dziwani kuti Allah Ngwaukali polanga. | Negative | 43 |
Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino." | Positive | 44 |
Kumwamba kapena kwa anthu?" | Positive | 45 |
Ngati helo alidi malo ozunzirako anthu, m'pake kuopa. | Negative | 46 |
"Kenako kudzanenedwa kwa amene adachita zoipa: "Lawani chilango chamuyaya! | Negative | 47 |
"Ndipo Ayah Zathu zikawerengcdwa kwa iwo zolongosola chilichonse momveka, alibe mtsutso wina koma kunena kuti: "Tibweretsereni makolo Athu (aukitseni akhale ndi moyo) ngati inu muli owona!" | Positive | 48 |
""Kupatula akapolo Anu omwe ali osankhidwa (oyeretsedwa) mwa iwo. | Positive | 49 |
"Nena: "E inu amene mudapatsidwa buku! chifukwa chiyani mukuzikana zizindikiro za Allah pomwe Allah ndi Mboni wa zonse zimene mukuchita?" | Negative | 50 |
Komabe, umboni wosatulutsa mawu wa zinthu zakumwamba ndi wamphamvu kwambiri. | Positive | 51 |
Kotero kodi izo kutsatira kuti ife kuba, ku nyumba ya mbuye wanu, golide kapena siliva? | Negative | 52 |
Ndithu taphunzitsidwa (mpaka tikudziwa) chiyankhulo cha mbalame, ndiponso tapatsidwa chilichonse; ndithu umenewu ndiubwino wopenyeka. | Positive | 53 |
Yosefe atawaona, anazindikira kuti akuda nkhawa ndi zinazake ndipo anawafunsa kuti: "N'chifukwa chiyani nkhope zanu zili zachisoni lero?" | Negative | 54 |
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndiloona, ndipo Inu Ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse." | Positive | 55 |
"Ndipo tidampulumutsa iye ndi anthu ake ku vuto lalikulu. | Positive | 56 |
Ngati ndinu wachinyamata ndipo mwakumana ndi zimenezi, muyenera kuganizira za Mose. | Negative | 57 |
Kodi sakuona kuti ilo (fano lawolo) silikuwalankhula ndiponso silikuwaongolera njira (yabwino?) | Negative | 58 |
"Ndithudi, taona kutembenukatembenuka kwa nkhope yako (kuyang'ana) kumwamba. | Positive | 59 |
Ambuye ali pafupi." | Positive | 60 |
Choncho Mulungu anamulanga ndi matenda oopsa akhate. | Negative | 61 |
Ndipo ndithu, lonjezo lanu ndiloona, ndipo inu ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse." | Positive | 62 |
"Onse awa, (abwino ndi oipa), timawapatsa awa ndi awa mwazopatsa za Mbuye wako; ndipo zopatsa za Mbuye wako sizotsekerezedwa (kuti zisamfike kapolo Wake). | Positive | 63 |
Chonchotu, atibweretsere chizizwa monga mmene adatumiziridwa (aneneri) oyamba." | Negative | 64 |
Ameneyu ndiye mwamuwona kuti ndiye wofunika punishment? | Negative | 65 |
Taonani,"Iye anati, "Moto ndi nkhuni. | Positive | 66 |
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa masiku a njala. | Negative | 67 |
Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?" | Negative | 68 |
Mbuye wako wanena (kuti): 'Izi nzofewa kwa Ine; ndithu ndidakulenga kale pomwe iwe sudali kanthu." | Positive | 69 |
"Kamuuzeni mawu ofewa mwina akalingalira (uthengawo) kapena akaopa. | Positive | 70 |
"Ndipo (Nuh) adati: "Kwerani m'menemo mwadzina la Allah mkuyenda kwake ndi mkukocheza kwake. | Positive | 71 |
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala | Negative | 72 |
Pamene muwerenga, kumbukirani ndi uthenga wa Mulungu kwa inu ngati munthu. | Positive | 73 |
"Ndipo tidawagawa iwo m'mafuko khumi ndi awiri (osiyanasiyana) monga mitundu ikuluikulu. | Negative | 74 |
mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina, | Positive | 75 |
"Ndipo mwa amene tidawalenga, alipo anthu oongolera (anzawo) ku choonadi. | Positive | 76 |
Kapena angachite mantha kuti zidzawavuta kuchita zimene Mulungu amafuna akadzabatizidwa. | Negative | 77 |
N'chifukwa chiyani wangokhala wekha kupereka ziweruzo ndipo anthu onse ali chiimire pamaso pako kuyambira m'mawa mpaka madzulo?" | Negative | 78 |
Atamuuza vutoli, Yesu anamuuza momveka bwino kuti: "Inu mumalambira chimene simuchidziwa." | Positive | 79 |
Ndiponso sadzawayeretsa (kumachimo awo); ndipo iwo adzapeza chilango chopweteka. | Negative | 80 |
monga mawu omveka, pamene khoma limodzi limaphimbidwa; | Negative | 81 |
Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza." | Negative | 82 |
Mwachitsanzo, Solomo anachonderera Mulungu kuti aziyankha mapembedzero a olambira Ake. | Positive | 83 |
mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. | Positive | 84 |
Ndipo, ndithudi, ngati pali mwamuna mu aquarium iyi. | Negative | 85 |
Iwo sayenera amafanana zovala zachimuna kapena zovala za osakhulupirira. | Negative | 86 |
"Pamene m'bale wawo (Mneneri) Hûd adawafunsa kuti: "Kodi simuopa (Allah)?" | Positive | 87 |
"Kufikira pamene adzatidzera (tsiku la Qiyâma, uku akulowetsedwa ku Moto). | Positive | 88 |
Atate, ndipulumutseni Ine ku nthaŵi iyi." | Negative | 89 |
"Mawa lino adzadziwa (tsiku lakuwatsikira chilango,) kuti ndiyani wabodza wodzitukumula (iwo kapena Swaleh). | Negative | 90 |
"Nena: "Yendani pa dziko ndi kuona momwe Allah adayambitsira chilengedwe; kenako Allah adzaumba, kuumba kwina. | Positive | 91 |
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu. | Negative | 92 |
Amphaka ngati dzina lawo limveka; | Positive | 93 |
"Kotero alemekezeke Yemwe m'manja Mwake muli ulamuliro pa chinthu chilichonse; ndipo kwa Iye (ndiko) mudzabweerera nonse. | Positive | 94 |
"Zimenezo nchifukwa chakuti iwo adakonda moyo wa dziko lapansi kwambiri kuposa wa pambuyo pa imfa; ndi kutinso Allah saongola anthu osakhulupirira. | Negative | 95 |
M'nthaka muli zizindikiro kwa Otsimikiza, (Zosonyeza kuti Mulungu alipo). | Positive | 96 |
ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka. | Positive | 97 |
Uchiteni mzinda uwu (wa Makka) kukhala wa mtendere; ndipo ndipatuleni ine ndi ana anga ku machitidwe opembedza mafano." | Positive | 98 |
Zikomo...izo anali Old School. | Positive | 99 |
Chichewa Sentiment Corpus
Dataset Description
This dataset contains sentiment-labeled text data in Chichewa for binary sentiment classification (Positive/Negative). Sentiments are extracted and processed from the English meanings of the sentences using DistilBERT for sentiment classification. The dataset is part of a larger collection of African language sentiment analysis resources.
Dataset Statistics
- Total samples: 834,916
- Positive sentiment: 450225 (53.9%)
- Negative sentiment: 384691 (46.1%)
Dataset Structure
Data Fields
- Text Column: Contains the original text in Chichewa
- sentiment: Sentiment label (Positive or Negative only)
Data Splits
This dataset contains a single split with all the processed data.
Data Processing
The sentiment labels were generated using:
- Model:
distilbert-base-uncased-finetuned-sst-2-english
- Processing: Batch processing with optimization for efficiency
- Deduplication: Duplicate entries were removed based on text content
- Filtering: Only Positive and Negative sentiments retained for binary classification
Usage
from datasets import load_dataset
# Load the dataset
dataset = load_dataset("michsethowusu/chichewa-sentiments-corpus")
# Access the data
print(dataset['train'][0])
# Check sentiment distribution
from collections import Counter
sentiments = [item['sentiment'] for item in dataset['train']]
print(Counter(sentiments))
Use Cases
This dataset is ideal for:
- Binary sentiment classification tasks
- Training sentiment analysis models for Chichewa
- Cross-lingual sentiment analysis research
- African language NLP model development
Citation
If you use this dataset in your research, please cite:
@dataset{chichewa_sentiments_corpus,
title={Chichewa Sentiment Corpus},
author={Mich-Seth Owusu},
year={2025},
url={https://huggingface.co/datasets/michsethowusu/chichewa-sentiments-corpus}
}
License
This dataset is released under the MIT License.
Contact
For questions or issues regarding this dataset, please open an issue on the dataset repository.
Dataset Creation
Date: 2025-07-02 Processing Pipeline: Automated sentiment analysis using HuggingFace Transformers Quality Control: Deduplication, batch processing optimizations, and binary sentiment filtering applied
- Downloads last month
- 0