Chichewa
stringlengths
10
500
sentiment
stringclasses
2 values
__index_level_0__
int64
0
835k
"Omwe unapangana nawo chipangano kenako naaswa chipangano chawo panthawi iliyonse (imene mwapangana), ndiponso iwo saopa Allah.
Positive
100
Ndipo amene angamenye nkhondo pa njira ya Allah, kenako ndikuphedwa kapena kupambana tidzampatsa malipiro aakulu.
Positive
101
"Tero ndithu tikadakulawitsa chilango chachikulu cha moyo (wa pa dziko lapansi) ndi chilango chachikulu utafa; kenako siukadapeza mthandizi wokupulumutsa kwa Ife.
Negative
102
Iwo ali ndi ana aamuna anayi, ndipo onse ali m'choonadi.
Positive
103
Tero, Allah waikhotetsa mitima yawo chifukwa chakuti iwo ndi anthu osazindikira.
Negative
104
Kenako anayankha kuti: "Inde, amunawo anabweradi kwa ine, koma sindinadziwe kuti achokera kuti.
Negative
105
Iye akuti: "Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthaŵa kulanga kwake kwa gehena?"
Negative
106
Ndipo Mbuye wako wakwana kukhala muongoli ndi mthandizi (wako).
Positive
107
Timasonyezanso kuti tikutsanzira chikhulupiriro cha Yosefe komanso kuti tikutsanzira Yehova, yemwe ndi wachifundo.
Positive
108
"Allah adzati: "Ili ndi tsiku lomwe olankhula zoona kudzawathandiza kuona kwawo.
Positive
109
Ndipo amene adachita zoipa, phokoso lidawachotsa moyo, tero kudawachera m'nyumba zawo ali lambilambi (atafa).
Negative
110
Waphunzitsa munthu zinthu (Zambiri) zomwe (iye) sadali Kuzidziwa.
Positive
111
Michael Lidzakhala dzina lake ngati adabadwira ku France.
Positive
112
Tilandireni (ntchito yathuyi), ndithudi, Inu ndinu Akumva; Odziwa."
Positive
113
"Ndipo tsiku la Qiyâma udzawaona omwe adamnamizira Allah, nkhope zawo zili zakuda.
Positive
114
Sanakumbukira dzanja lake, tsikuli anawawombola kwa msautsi.
Negative
115
Kapena mudafuna kuti mkwiyo ukutsikireni kuchokera kwa Mbuye wanu; tero mwaswa lonjezo langa"?
Negative
116
Tikuwalipirira anthu osalungama.
Positive
117
Sinditsatira Koma zokhazo zimene zikuvumbulutsidwa Kwa ine; ndipo ine sindili kanthu koma Mchenjezi wolongosola (Zofunika) ."
Negative
118
Sinditsatira koma zokhazo zimene zikuvumbulutsidwa kwa ine; ndipo ine sindili kanthu koma mchenjezi wolongosola (zofunika)."
Negative
119
Ndipo mulole iwo kuonjezera mu unyinji kudutsa dziko lapansi. "
Positive
120
Ndikuganiza kuti ziyenera kukhala patsamba la aliyense, Patric.
Negative
121
Ndikuti usiku umenewo ngwabwino kuposa miyezi chikwi chimodzi.
Negative
122
"Moyo wa pa dziko lapansi wakometsedwa kwa amene sadakhulupirire, ndipo amawachitira chipongwe amene akhulupirira.
Positive
123
""Ndipo tadza kwa iwe ndi (chinthu) choonadicho, ndithu ife ndi owona (pazimene tinenazi)."
Positive
124
(Mneneri Mûsa) adati: "Ndithudi, inu ndinu anthu osazindikira."
Negative
125
Kodi mukutsutsana naye (Mthenga wa Mulungu) pazimene adaziona.
Negative
126
Ndipo ndalamulidwa kukhala mmodzi wa okhulupirira."
Positive
127
(Luti) adati: "Ndithudi, inu
Positive
128
Koma sizinthu zakumwamba, mwachitsanzo, angelo, gawo la chilengedwe.
Positive
129
Chamunthu) ndi wosaumbidwa,
Negative
130
" (Iblis) adanena: "Ine ndine wabwino kuposa iye (Adam); chifukwa ine mudandilenga kuchokera ku Moto, ndipo iye mudamulenga kuchokera kudongo."
Positive
131
koma njira ya munthu wolungama ili ngati msewu waukulu.
Positive
132
ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake.
Positive
133
Ndipo ine sindingathamangitse amene akhulupirira (monga momwe mudandipemphera kuti ndiwathamangitse anthu ofooka kuti inu mulowe m'malo mwawo), ndithu iwo adzakumana ndi Mbuye wawo, ndipo ine ndikukuonani monga anthu osazindikira (mbuli)."
Negative
134
Koma pamene (pakatipo) padalemera (patangotsala pang'ono kuti abereke) anampempha Allah, Mbuye wawo (kuti): "Ngati mutipatsa mwana wabwino, ndithu tidzakhala mwa othokoza kwambiri."
Positive
135
Muolowetsa dzanja lanu, nimukwaniritsira zamoyo zonse chokhumba chawo."
Positive
136
"Ndipo musakhale monga aja achinyengo omwe akunena: "Tamva (choonadi ndipo tachisunga)," pomwe iwo sakumva (kumva kochigonjera).
Negative
137
"Ndipo masautso akampeza munthu, amapempha Mbuye wake ndi kutembenukira kwa Iye (pomwe chikhalirecho adali kumnyoza).
Positive
138
Mariya anati: 'Kodi zimenezi zingatheke bwanji?
Negative
139
Mafunso aliwonse atha kupita ku Federal Protective Service. "
Negative
140
Ndidzakhala naye m'nthawi ya masautso."
Positive
141
Koma Allah akufuna kuchitsimikiza choonadi ndi mawu Ake ndi kudula mizu ya osakhulupirira, (pomenyana ndi gulu lamphamvulo, omwe ndi ankhondo a Chikuraishi).
Negative
142
Nena: "Utsogozi weniweni ngwa Allah, ndipo talamulidwa kuti tigonjere Mbuye wa zolengedwa zonse."
Negative
143
Iye anati: "Njoka inu, ana a mphiri, mudzathawa bwanji chiweruzo cha Gehena?"
Negative
144
Ndipo ine ndine mmodzi mwa Asilamu (omugonjera monga iwo akumgonjera)."
Positive
145
Fanizo la mkazi ndi ndalama yotayika likutiuza chochita.
Positive
146
Ndipo tidampatsa nzeru ali mwana.
Positive
147
Ndipo pa munthu: Zimachotsa madalitso a moyo wa munthu,
Positive
148
Anali atalonjeza kuti adzapangitsa kuti ana a Yakobo akhale mtundu waukulu.
Positive
149
Nena (kwa iwo): "Zimene zili kwa Allah nzabwino kwa inu kuposa masewero ndi malonda.
Negative
150
"Sad, ndikulumbira Qur'an (iyi) ya ulaliki (wothandiza).
Negative
151
Iye (Allah) sakonda opyoza muyeso (oononga).
Negative
152
"Choncho ndidati (kwa anthu anga): Pemphani kwa Mbuye wanu chikhululuko (pa kukana kwanu ndi kutonza kwanu), ndithu Iye ali Wokhululuka kwambiri.
Negative
153
Tikhoza kungokhudza mitu yochepa yokha m'mawa uno yokhudza Kristu Yesu Mwini.
Positive
154
"Ndipo (Mûsa) pamene adakula nsinkhu wake ndi kulingana bwino tidampatsa nzeru ndi maphunziro.
Positive
155
""Atsateni omwe sakupemphani malipiro (pa kukulangizani kwawo), ndipo iwo ngoongoka."
Positive
156
Choncho, nena: "Kodi bwanji simukumuopa?"
Positive
157
"Asiye azidya (chakudya monga momwe zidyera nyama) ndi kusangalala; ndipo chiyembekezo chiziwatangwanitsa ndi kuwanyenga; posachedwa adziwa (kuti zimene amaziyembekezerazo nzabodza).
Positive
158
Kodi iye angafanane ndi yemwe akulamula mwa chilungamo, yemwenso ali pa njira yolunjika?
Positive
159
Otsalira adzatembenuzira kumbuyo, otsalira a Yakobo, kwa Mulungu Wamphamvu.
Positive
160
" (Ayuda) sangamenyane ndi inu ali pa gulu kupatula m'midzi yotetezedwa ndi malinga, kapena kuseri kwa zipupa.
Negative
161
"Pamene adawauza Nuh m'bale wawo kuti: "Kodi simukuopa (Allah ngakhale nditakuuzani zoopsa zimene zikukudikirani)?"
Positive
162
Yakobo ankayesetsa kuchita zonse zimene akanatha kuti adalitsidwe ndi Mulungu ngakhale kuti ankakumana ndi mavuto ena.
Positive
163
Friday wabwino News wabwino kwa ochimwa monga inu ndi ine.
Positive
164
Nakuti ule omwe an'bzicepsa pakati panupa, umweyo ndiye nkulu."
Positive
165
Ndithu Allah akufuna kuwalanga ndi zimenezo pa dziko lapansi, ndi kuti mizimu yawo ichoke ali osakhulupirira.
Negative
166
Ndithu nzoipa kwabasi zomwe iwo akhala akuchita.
Negative
167
"Kodi akuganiza kuti tikamawapatsa chuma ndi ana,
Negative
168
Tsiku lakudza zina mwa zizindikiro za Mbuye wako, munthu (wosakhulupirira) chikhulupiliro chake (panthawiyo) sichidzamthandiza, yemwe sadakhulupirirepo kale, kapena (msilamu) yemwe sanapindule nacho chikhulupiliro chake.
Negative
169
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndi lowona, Ndipo Inu ndi oweruza mwachowonadi kuposa aweruzi onse."
Positive
170
Ndithu, Ife tamlenga munthu kuchokera Kumbewu ya umunthu yosanganikirana (Ya mkazi ndi ya mwamuna) kuti Timuyese mayeso (ndi malamulo Athu); Choncho tidampanga kukhala wakumva Ndi wopenya; (amve mawu a Mulungu) Ndi kuti aone zisonyezo Zake).
Positive
171
Palibe ayenera kupulumutsidwa ndi kubwezeretsedwa kwa Mulungu, kotero Iye anali wachisomo kuombola anthu ku Israel.
Negative
172
"Ndipo akadayesa kumenyana nanu amene sadakhulupirire; akadatembenuza misana kuthawa; kenako sakadapeza mthandizi kapena mtetezi.
Negative
173
Iyi ndi sura; Taivumbulutsa,
Positive
174
Kodi wadya zipatso za mtengo umene ndinakulamulira kuti usadye?"
Negative
175
Ndipo ngati anyozera dziwa kuti Allah afuna kuwapatsa chilango cha ena mwa machimo awo.
Negative
176
Munthu adzanena tsiku limenelo: "Nkuti kothawira (chilangochi?) "
Negative
177
Ndiye kuti palibe chomwe chatsala, koma zonse ndi za mthenga.
Positive
178
Nena: "Allah ndi Yemwe akuyambitsa zolengedwa kenaka ndi kuzibweza (pambuyo poonongeka).
Positive
179
" (Farawo) adati: "Inde, (ndipo kuonjezera apo) ndithu inu mudzakhala mwa amene amakhala pafupi (ndi ine, monga nduna zanga)."
Positive
180
Zedi, zitsanzo adzapelekedwa mlanduwo zitsanzo 'ndi zingati mthenga mwa inu.
Negative
181
"Nena: "Simudzafunsidwa pa zimene (ife) talakwa, nafenso sitidzafunsidwa pazimene mukuchita."
Positive
182
Taonani, mapazi a iwo amene adayika mwamuna wako ali pakhomo, ndipo adzakunyamula iwe kuchokera!"
Positive
183
Kodi bwanji sadatumizidwe mngelo kwa iye kuti azikhala naye limodzi uku akuchenjeza?"
Negative
184
Ndipamene ndinawatsekereza ana a Israyeli kwa iwe (kuti asakuzunze) pamene udawadzera ndi zisonyezo zooneka, ndipo aja mwa iwo omwe sadakhulupirire, adati: "Ichi sichina, koma ndi matsenga owonekera."
Positive
185
Choncho mdzadziwa mmene lilili chenjezo Langa (pa inu).
Negative
186
"Kapena tidawapatsa buku lina tisadapereke ili, kotero kuti iwo agwiritsitsa limenelo (ndi kugwirizana nazo zili mmenemo)?
Negative
187
Ngati utichotsera chilangochi, ndithudi tikukhulupirira, ndipo tiwatumiza pamodzi nawe ana a Israyeli (kuti unke nawo kumene ukufuna)."
Positive
188
Ndithudi, zimene zavumbulutsidwa kwa iwe kuchokera kwa Mbuye wako, ziwaonjezera ambiri a iwo (Ayuda) kulumpha malire ndi kusakhulupirira.
Positive
189
"Ndipo ikawerengedwa kwa iwo Qur'an, sagwetsa pansi nkhope zawo (modzichepetsa).
Positive
190
"Ndipo sikotheka Qur'an iyi kukhala yopekedwa, yosachokera kwa Allah (monga momwe munenera).
Positive
191
munthu zinthu zomwe sadali kuzidziwa,
Negative
192
Mwachitsanzo, ku Andorra pazifukwa zina simungathe kupha anthu oposa awiri patsiku.
Positive
193
mtengezereni njira iye atsupaye dzulu ya maingu,
Positive
194
Ndiyeno iyo idzafika kumapeto a moyo wake ndipo sipadzapezeka woithandiza."
Negative
195
Kodi munganene bwanji zamwano chotere kwa ine?"
Negative
196
"Kapena muli nawo mapangano ndi Ife okafika mpaka tsiku lachimaliziro akuti inu mudzapeza zimene mukudziweruzira?
Negative
197
Ndipo ndithu Allah ali pamodzi ndi ochita zabwino.
Positive
198
" (Ndipo tidzawauza) "Lowani m'menemo mwamtendere, mosatekeseka."
Positive
199