Chichewa
stringlengths 10
500
| sentiment
stringclasses 2
values | __index_level_0__
int64 0
835k
|
---|---|---|
"Omwe unapangana nawo chipangano kenako naaswa chipangano chawo panthawi iliyonse (imene mwapangana), ndiponso iwo saopa Allah. | Positive | 100 |
Ndipo amene angamenye nkhondo pa njira ya Allah, kenako ndikuphedwa kapena kupambana tidzampatsa malipiro aakulu. | Positive | 101 |
"Tero ndithu tikadakulawitsa chilango chachikulu cha moyo (wa pa dziko lapansi) ndi chilango chachikulu utafa; kenako siukadapeza mthandizi wokupulumutsa kwa Ife. | Negative | 102 |
Iwo ali ndi ana aamuna anayi, ndipo onse ali m'choonadi. | Positive | 103 |
Tero, Allah waikhotetsa mitima yawo chifukwa chakuti iwo ndi anthu osazindikira. | Negative | 104 |
Kenako anayankha kuti: "Inde, amunawo anabweradi kwa ine, koma sindinadziwe kuti achokera kuti. | Negative | 105 |
Iye akuti: "Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthaŵa kulanga kwake kwa gehena?" | Negative | 106 |
Ndipo Mbuye wako wakwana kukhala muongoli ndi mthandizi (wako). | Positive | 107 |
Timasonyezanso kuti tikutsanzira chikhulupiriro cha Yosefe komanso kuti tikutsanzira Yehova, yemwe ndi wachifundo. | Positive | 108 |
"Allah adzati: "Ili ndi tsiku lomwe olankhula zoona kudzawathandiza kuona kwawo. | Positive | 109 |
Ndipo amene adachita zoipa, phokoso lidawachotsa moyo, tero kudawachera m'nyumba zawo ali lambilambi (atafa). | Negative | 110 |
Waphunzitsa munthu zinthu (Zambiri) zomwe (iye) sadali Kuzidziwa. | Positive | 111 |
Michael Lidzakhala dzina lake ngati adabadwira ku France. | Positive | 112 |
Tilandireni (ntchito yathuyi), ndithudi, Inu ndinu Akumva; Odziwa." | Positive | 113 |
"Ndipo tsiku la Qiyâma udzawaona omwe adamnamizira Allah, nkhope zawo zili zakuda. | Positive | 114 |
Sanakumbukira dzanja lake, tsikuli anawawombola kwa msautsi. | Negative | 115 |
Kapena mudafuna kuti mkwiyo ukutsikireni kuchokera kwa Mbuye wanu; tero mwaswa lonjezo langa"? | Negative | 116 |
Tikuwalipirira anthu osalungama. | Positive | 117 |
Sinditsatira Koma zokhazo zimene zikuvumbulutsidwa Kwa ine; ndipo ine sindili kanthu koma Mchenjezi wolongosola (Zofunika) ." | Negative | 118 |
Sinditsatira koma zokhazo zimene zikuvumbulutsidwa kwa ine; ndipo ine sindili kanthu koma mchenjezi wolongosola (zofunika)." | Negative | 119 |
Ndipo mulole iwo kuonjezera mu unyinji kudutsa dziko lapansi. " | Positive | 120 |
Ndikuganiza kuti ziyenera kukhala patsamba la aliyense, Patric. | Negative | 121 |
Ndikuti usiku umenewo ngwabwino kuposa miyezi chikwi chimodzi. | Negative | 122 |
"Moyo wa pa dziko lapansi wakometsedwa kwa amene sadakhulupirire, ndipo amawachitira chipongwe amene akhulupirira. | Positive | 123 |
""Ndipo tadza kwa iwe ndi (chinthu) choonadicho, ndithu ife ndi owona (pazimene tinenazi)." | Positive | 124 |
(Mneneri Mûsa) adati: "Ndithudi, inu ndinu anthu osazindikira." | Negative | 125 |
Kodi mukutsutsana naye (Mthenga wa Mulungu) pazimene adaziona. | Negative | 126 |
Ndipo ndalamulidwa kukhala mmodzi wa okhulupirira." | Positive | 127 |
(Luti) adati: "Ndithudi, inu | Positive | 128 |
Koma sizinthu zakumwamba, mwachitsanzo, angelo, gawo la chilengedwe. | Positive | 129 |
Chamunthu) ndi wosaumbidwa, | Negative | 130 |
" (Iblis) adanena: "Ine ndine wabwino kuposa iye (Adam); chifukwa ine mudandilenga kuchokera ku Moto, ndipo iye mudamulenga kuchokera kudongo." | Positive | 131 |
koma njira ya munthu wolungama ili ngati msewu waukulu. | Positive | 132 |
ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake. | Positive | 133 |
Ndipo ine sindingathamangitse amene akhulupirira (monga momwe mudandipemphera kuti ndiwathamangitse anthu ofooka kuti inu mulowe m'malo mwawo), ndithu iwo adzakumana ndi Mbuye wawo, ndipo ine ndikukuonani monga anthu osazindikira (mbuli)." | Negative | 134 |
Koma pamene (pakatipo) padalemera (patangotsala pang'ono kuti abereke) anampempha Allah, Mbuye wawo (kuti): "Ngati mutipatsa mwana wabwino, ndithu tidzakhala mwa othokoza kwambiri." | Positive | 135 |
Muolowetsa dzanja lanu, nimukwaniritsira zamoyo zonse chokhumba chawo." | Positive | 136 |
"Ndipo musakhale monga aja achinyengo omwe akunena: "Tamva (choonadi ndipo tachisunga)," pomwe iwo sakumva (kumva kochigonjera). | Negative | 137 |
"Ndipo masautso akampeza munthu, amapempha Mbuye wake ndi kutembenukira kwa Iye (pomwe chikhalirecho adali kumnyoza). | Positive | 138 |
Mariya anati: 'Kodi zimenezi zingatheke bwanji? | Negative | 139 |
Mafunso aliwonse atha kupita ku Federal Protective Service. " | Negative | 140 |
Ndidzakhala naye m'nthawi ya masautso." | Positive | 141 |
Koma Allah akufuna kuchitsimikiza choonadi ndi mawu Ake ndi kudula mizu ya osakhulupirira, (pomenyana ndi gulu lamphamvulo, omwe ndi ankhondo a Chikuraishi). | Negative | 142 |
Nena: "Utsogozi weniweni ngwa Allah, ndipo talamulidwa kuti tigonjere Mbuye wa zolengedwa zonse." | Negative | 143 |
Iye anati: "Njoka inu, ana a mphiri, mudzathawa bwanji chiweruzo cha Gehena?" | Negative | 144 |
Ndipo ine ndine mmodzi mwa Asilamu (omugonjera monga iwo akumgonjera)." | Positive | 145 |
Fanizo la mkazi ndi ndalama yotayika likutiuza chochita. | Positive | 146 |
Ndipo tidampatsa nzeru ali mwana. | Positive | 147 |
Ndipo pa munthu: Zimachotsa madalitso a moyo wa munthu, | Positive | 148 |
Anali atalonjeza kuti adzapangitsa kuti ana a Yakobo akhale mtundu waukulu. | Positive | 149 |
Nena (kwa iwo): "Zimene zili kwa Allah nzabwino kwa inu kuposa masewero ndi malonda. | Negative | 150 |
"Sad, ndikulumbira Qur'an (iyi) ya ulaliki (wothandiza). | Negative | 151 |
Iye (Allah) sakonda opyoza muyeso (oononga). | Negative | 152 |
"Choncho ndidati (kwa anthu anga): Pemphani kwa Mbuye wanu chikhululuko (pa kukana kwanu ndi kutonza kwanu), ndithu Iye ali Wokhululuka kwambiri. | Negative | 153 |
Tikhoza kungokhudza mitu yochepa yokha m'mawa uno yokhudza Kristu Yesu Mwini. | Positive | 154 |
"Ndipo (Mûsa) pamene adakula nsinkhu wake ndi kulingana bwino tidampatsa nzeru ndi maphunziro. | Positive | 155 |
""Atsateni omwe sakupemphani malipiro (pa kukulangizani kwawo), ndipo iwo ngoongoka." | Positive | 156 |
Choncho, nena: "Kodi bwanji simukumuopa?" | Positive | 157 |
"Asiye azidya (chakudya monga momwe zidyera nyama) ndi kusangalala; ndipo chiyembekezo chiziwatangwanitsa ndi kuwanyenga; posachedwa adziwa (kuti zimene amaziyembekezerazo nzabodza). | Positive | 158 |
Kodi iye angafanane ndi yemwe akulamula mwa chilungamo, yemwenso ali pa njira yolunjika? | Positive | 159 |
Otsalira adzatembenuzira kumbuyo, otsalira a Yakobo, kwa Mulungu Wamphamvu. | Positive | 160 |
" (Ayuda) sangamenyane ndi inu ali pa gulu kupatula m'midzi yotetezedwa ndi malinga, kapena kuseri kwa zipupa. | Negative | 161 |
"Pamene adawauza Nuh m'bale wawo kuti: "Kodi simukuopa (Allah ngakhale nditakuuzani zoopsa zimene zikukudikirani)?" | Positive | 162 |
Yakobo ankayesetsa kuchita zonse zimene akanatha kuti adalitsidwe ndi Mulungu ngakhale kuti ankakumana ndi mavuto ena. | Positive | 163 |
Friday wabwino News wabwino kwa ochimwa monga inu ndi ine. | Positive | 164 |
Nakuti ule omwe an'bzicepsa pakati panupa, umweyo ndiye nkulu." | Positive | 165 |
Ndithu Allah akufuna kuwalanga ndi zimenezo pa dziko lapansi, ndi kuti mizimu yawo ichoke ali osakhulupirira. | Negative | 166 |
Ndithu nzoipa kwabasi zomwe iwo akhala akuchita. | Negative | 167 |
"Kodi akuganiza kuti tikamawapatsa chuma ndi ana, | Negative | 168 |
Tsiku lakudza zina mwa zizindikiro za Mbuye wako, munthu (wosakhulupirira) chikhulupiliro chake (panthawiyo) sichidzamthandiza, yemwe sadakhulupirirepo kale, kapena (msilamu) yemwe sanapindule nacho chikhulupiliro chake. | Negative | 169 |
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndi lowona, Ndipo Inu ndi oweruza mwachowonadi kuposa aweruzi onse." | Positive | 170 |
Ndithu, Ife tamlenga munthu kuchokera Kumbewu ya umunthu yosanganikirana (Ya mkazi ndi ya mwamuna) kuti Timuyese mayeso (ndi malamulo Athu); Choncho tidampanga kukhala wakumva Ndi wopenya; (amve mawu a Mulungu) Ndi kuti aone zisonyezo Zake). | Positive | 171 |
Palibe ayenera kupulumutsidwa ndi kubwezeretsedwa kwa Mulungu, kotero Iye anali wachisomo kuombola anthu ku Israel. | Negative | 172 |
"Ndipo akadayesa kumenyana nanu amene sadakhulupirire; akadatembenuza misana kuthawa; kenako sakadapeza mthandizi kapena mtetezi. | Negative | 173 |
Iyi ndi sura; Taivumbulutsa, | Positive | 174 |
Kodi wadya zipatso za mtengo umene ndinakulamulira kuti usadye?" | Negative | 175 |
Ndipo ngati anyozera dziwa kuti Allah afuna kuwapatsa chilango cha ena mwa machimo awo. | Negative | 176 |
Munthu adzanena tsiku limenelo: "Nkuti kothawira (chilangochi?) " | Negative | 177 |
Ndiye kuti palibe chomwe chatsala, koma zonse ndi za mthenga. | Positive | 178 |
Nena: "Allah ndi Yemwe akuyambitsa zolengedwa kenaka ndi kuzibweza (pambuyo poonongeka). | Positive | 179 |
" (Farawo) adati: "Inde, (ndipo kuonjezera apo) ndithu inu mudzakhala mwa amene amakhala pafupi (ndi ine, monga nduna zanga)." | Positive | 180 |
Zedi, zitsanzo adzapelekedwa mlanduwo zitsanzo 'ndi zingati mthenga mwa inu. | Negative | 181 |
"Nena: "Simudzafunsidwa pa zimene (ife) talakwa, nafenso sitidzafunsidwa pazimene mukuchita." | Positive | 182 |
Taonani, mapazi a iwo amene adayika mwamuna wako ali pakhomo, ndipo adzakunyamula iwe kuchokera!" | Positive | 183 |
Kodi bwanji sadatumizidwe mngelo kwa iye kuti azikhala naye limodzi uku akuchenjeza?" | Negative | 184 |
Ndipamene ndinawatsekereza ana a Israyeli kwa iwe (kuti asakuzunze) pamene udawadzera ndi zisonyezo zooneka, ndipo aja mwa iwo omwe sadakhulupirire, adati: "Ichi sichina, koma ndi matsenga owonekera." | Positive | 185 |
Choncho mdzadziwa mmene lilili chenjezo Langa (pa inu). | Negative | 186 |
"Kapena tidawapatsa buku lina tisadapereke ili, kotero kuti iwo agwiritsitsa limenelo (ndi kugwirizana nazo zili mmenemo)? | Negative | 187 |
Ngati utichotsera chilangochi, ndithudi tikukhulupirira, ndipo tiwatumiza pamodzi nawe ana a Israyeli (kuti unke nawo kumene ukufuna)." | Positive | 188 |
Ndithudi, zimene zavumbulutsidwa kwa iwe kuchokera kwa Mbuye wako, ziwaonjezera ambiri a iwo (Ayuda) kulumpha malire ndi kusakhulupirira. | Positive | 189 |
"Ndipo ikawerengedwa kwa iwo Qur'an, sagwetsa pansi nkhope zawo (modzichepetsa). | Positive | 190 |
"Ndipo sikotheka Qur'an iyi kukhala yopekedwa, yosachokera kwa Allah (monga momwe munenera). | Positive | 191 |
munthu zinthu zomwe sadali kuzidziwa, | Negative | 192 |
Mwachitsanzo, ku Andorra pazifukwa zina simungathe kupha anthu oposa awiri patsiku. | Positive | 193 |
mtengezereni njira iye atsupaye dzulu ya maingu, | Positive | 194 |
Ndiyeno iyo idzafika kumapeto a moyo wake ndipo sipadzapezeka woithandiza." | Negative | 195 |
Kodi munganene bwanji zamwano chotere kwa ine?" | Negative | 196 |
"Kapena muli nawo mapangano ndi Ife okafika mpaka tsiku lachimaliziro akuti inu mudzapeza zimene mukudziweruzira? | Negative | 197 |
Ndipo ndithu Allah ali pamodzi ndi ochita zabwino. | Positive | 198 |
" (Ndipo tidzawauza) "Lowani m'menemo mwamtendere, mosatekeseka." | Positive | 199 |
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.