Chichewa
stringlengths
10
500
sentiment
stringclasses
2 values
__index_level_0__
int64
0
835k
Kenako tinaona kalavani inayake yakutha.
Negative
200
Ndikuganiza kuti ukunena zowona, Aaron.
Positive
201
"Ndipo akutiponyera fanizo (lotsutsa kukhoza Kwathu kuukitsa akufa) ndi kuiwala chilengedwe chake (chochokera kumadzi opanda pake).
Negative
202
Koma dziwani izi: Mukandipha, mudzakhala mukupha munthu wosalakwa.'
Negative
203
Kodi nanunso mwapeza zomwe Mbuye wanu adakulonjezani kuti nzoona?"
Positive
204
"Koma amene angafune (zina) kusiya zimenezi iwowo ndiwo olumpha malire.
Positive
205
Tipatsirenitu gawo la chilango chathu lisanafike tsiku lachiwerengero."
Negative
206
Ndipo akakapempha chithandizo (chifukwa cha ludzu loopsya lomwe likawapeza), akathandizidwa popatsidwa madzi (otentha kwambiri) monga madzi a chitsulo chosungunuka, omwe adzasupula nkhope zawo.
Negative
207
Pakuti dzanja lanu linali kundilemera usana ndi usiku."
Positive
208
Yemwe angakhale connected ndi Qur'an, akhala wolemekezeka kuposa wina aliyense, chifukwa Allah analemekeza chilichonse chokhudzana ndi Qur'an.
Negative
209
Ndipo posachedwa adzawalipira pa zomwe adali kupeka.
Negative
210
Kumbukirani kuti analemba kuti: "Mulungu ali wamkulu woposa mitima yathu."
Positive
211
Pamapeto pa tsiku, banja liyenera kuiwala zonse - a Mark V. Olson.
Negative
212
"Kodi akukulonjezani kuti mukadzafa ndikusanduka dothi ndi mafupa, mudzaukitsidwanso (m'manda)?
Positive
213
Ndiye dzifunseni kuti, 'Kodi n'kutheka kuti Mulungu akugwiritsa ntchito anthu amenewa pofuna kundikokera kwa iye?'
Negative
214
"Sipadzakhala (china) koma mkuwe umodzi basi; adzangozindikira iwo onse atabweretsedwa patsogolo Pathu.
Positive
215
Iye anati: "Ndachita pangano ndi maso anga.
Positive
216
Kodi kunyumba kwa bambo ako kuli malo oti tikhoza kugonako?"
Negative
217
ndipo wolungama akhale motetezedwa.
Positive
218
Nena: "Zozizwitsa zili kwa Allah; ndipo ine ndine mchenjezi woonekera, (ndilibe mphamvu zokudzetserani zozizwitsa koma pokhapo Allah atafuna)."
Negative
219
Ndipo wawaikira nthawi (yodziwika) yopanda chikaiko, (yowaukitsira ku imfa).
Negative
220
"Kodi zidzakhala zotani pamene tidzawasonkhanitsa tsiku lopanda chikaiko?
Positive
221
"Kapena iwo ali nawo othandidzana nawo (pa mau awa)?
Negative
222
Onse adzabwerera kwa Ife.
Positive
223
Adzabwerera tsiku la nkhondo.
Positive
224
Ndipo amene atembenukire kutali (kunyoza iwe, ndiye kuti zoipa zili pa iye mwini).
Negative
225
" (Nena:) "Kodi ndifune woweruza wina kusiya Allah, pomwe Iye ndi Yemwe adavumbulutsa buku kwa inu lofotokoza chilichonse?"
Positive
226
"Kuti liwachenjeze amene ali moyo, ndi kuti litsimikizike liwu (la chilango) pa osakhulupirira.
Negative
227
Ndipo anthu untamed adzalowa izo, ndipo iwo aiipitse.
Negative
228
"Basi, kumbutsa (anthu) ndithu iwe, ndiwe mkumbutsi.
Positive
229
Komabe, "ikapezedwa idzabwezera kasanu ndi kaŵiri; idzapereka chuma chonse cha m'nyumba yake."
Negative
230
Zinali zosatheka, zinali m'magazi anga.
Negative
231
Kodi munthu akuganiza kuti Ife (Amene tidamlenga kuchokera Popanda chilichonse) sitidzatha Kusonkhanitsa mafupa ake (ofumbwa)?
Negative
232
"Ndipo ndithu alipo ena mwa inu otsalira m'mbuyo sapita ku nkhondo, (ndiponso amaletsa anzawo).
Negative
233
"Naipereka kwa iwo (koma sadadye); iye adanena (modabwa): "Kodi bwanji simukudya?"
Negative
234
"Ndithu Ine ndine Allah palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Ine; choncho ndipembeze, pemphera Swala moyenera pondikumbukira.
Positive
235
Ndipo mwaphunzitsidwa (ndi iyi Qur'an) zomwe simudali kuzidziwa, inu ngakhale makolo anu.
Negative
236
Ndiyendetseni m'njira yoona,
Positive
237
Koma osadandaula, Lena, zomwe ndidakwanitsabe kuwombera.
Positive
238
Pakuti ndaona kuti mukhale basi pamaso panga, mkati m'badwo uno.
Positive
239
Davide anali ndi zinthu zonsezi koma anakhala wodzichepetsa kwa moyo wake wonse.
Positive
240
Kapena yochokera Dead kapena Alive.
Negative
241
"Ndipo iwo akadakhulupirira nadzitchinjiriza (ku zoletsedwa), ndithudi, mphoto yochokera kwa Allah ikadakhala yabwino kwa iwo, akadadziwa.
Negative
242
Unali wangwiro m'njira zako chilengedwere iwe, mpaka chinapezeka mwa iwe chosalungama.
Negative
243
Koma popeza pa nthawiyi n'kuti dzina la Mulungu likudziwika kale, n'chifukwa chiyani Mose anafunsa funso limeneli?
Negative
244
"Ndithu amene adzadze kwa Mbuye wake uku ali wamachimo, adzapeza moto wa Jahannam; sadzafa m'menemo, ndipo sadzakhalanso ndi moyo wabwino.
Negative
245
Kodi ukuona chifukwa chake Mulungu anawononga anthuwo? - Iwo anali oipa, ndipo zimene ankaganiza zinali 'zoipa zokhazokha.'
Negative
246
"Akukufunsa za mowa ndi njuga.
Negative
247
Cifukwa cace, taonani, nditumiza kwa inu aneneri ndi anzeru ndi alembi.
Negative
248
"Adati: "Sichina ichi (Qur'an) koma ndi matsenga amene adalandiridwa (kuchokera kwa amatsenga akale),
Positive
249
mu maina Ake Iye Wapamwambamwamba,
Positive
250
Ngati akadamumvera Allah, ndithu zikadakhala zabwino kwa iwo.
Negative
251
"Auze amene sadakhulupirire: "Posachedwapa mugonjetsedwa ndi kusonkhanitsidwa ndi kuponyedwa ku Moto.
Negative
252
Iye anayankha kuti: "Inde, ndifedi Akristu chifukwa chakuti Yesu ndiye chitsanzo chathu.
Positive
253
Taonani, adzailowa kwa inu, ndipo mudzaona njira yawo ndi zimene anachita.
Positive
254
"M'nthaka muli zizindikiro kwa otsimikiza, (zosonyeza kuti Allah alipo).
Positive
255
""Pita ndi kalata yangayi, kaiponye kwa iwo; kenako ukadzipatule kwa iwo (ukakhale pambali) ndi kuona momwe azikayankhira."
Positive
256
Tsoka inu, chifukwa muli ngati manda achikumbutso osaonekera, moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!"
Negative
257
Ngati utsata zilakolako zawo pambuyo pa zomwe zakudzera, monga kuzindikira (kwenikweni), sudzapeza mtetezi aliyense ngakhale mthandizi kwa Allah.
Negative
258
Panopa Satana akuukira kwambiri anthu a Mulungu.
Negative
259
(Akawauza kuti): "Ndithu iyi ndi mphoto
Positive
260
Ndipo kum'bandakucha, iwo Amapempha chikhululuko.
Negative
261
Tikatero, mnzathuyo sadzavutika kutimvetsera.
Negative
262
Ndipo pamene mukuwapatsa chuma chawo, funani mboni (zoonelera kuperekedwa kwa chumacho).
Negative
263
"Komanso wochitira zabwino makolo ake ndipo sadali wodzitukumula (kwa anthu) kapena kunyoza (Allah).
Positive
264
"Choncho apewe (osakhulupirirawa) amene anyozera chikumbutso Chathu (Qur'an); ndipo palibe chimene akufuna koma moyo wa padziko lapansi basi.
Positive
265
Sindinawauze amayi ako zokwanira; Ndikanayenera kumamuuza tsiku lililonse chifukwa anali wangwiro tsiku lililonse.
Positive
266
Nena: "Nanga bwanji simukumuopa?"
Positive
267
Mtima wake wakhazikika, sadzaopa, kufikira adzaona adani ake.
Positive
268
Perekani chitsanzo cha "zakuya za Mulungu" zomwe gulu la kapolo lazifotokoza.
Positive
269
Kapena kudza zina mwa zizindikiro za Mbuye wako (zomwe adati zidzadza)?
Negative
270
"Ndipo adatuluka kuchipinda chopemphelera ndikuonekera kwa anthu ake, ndipo adawalozera (pomwe sadathe kuyankhula) kuti: "Lemekezani Allah m'mawa ndi madzulo."
Positive
271
""Ndipo Allah achilimbikitsa choonadi ndi mau Ake, ngakhale oipa anyansidwe nazo."
Positive
272
Mtsikana akhoza kukhala ndipo adzatchedwa yemweyo - Nastya.
Negative
273
pa dziko ndithudi umenewo ukuchokera kwa Iye Subhaanahu Wataalaa.
Positive
274
Kodi iwe ukuganiza kuti mwa aŵiriŵa ndani anasangalatsa Mulungu?
Positive
275
Ndimasulireni maloto angawa, ngati inu mumatha kumasulira maloto."
Positive
276
"Ena mwa inu mwawawona kale 'alonda athu apamwamba' kale.
Negative
277
""Ndithu takhulupirira Mbuye wathu kuti atikhululukire zolakwa zathu ndi matsenga amene watikakamiza (kuchita); ndipo Allah ndi Yemwe ali Wabwino ndi Wamuyaya (osati iwe)."
Positive
278
Ndipo taika chidani ndi kusakondana pakati pawo mpaka tsiku la chimariziro.
Negative
279
Ngati anamva zimenezi Dhamma, adzakhala ndi mwamsanga anamvetsa izo.'
Positive
280
"Kodi sadaone kuti (mwana wang'ombe) sabweza mawu kwa iwo, ndiponso sangathe kudzetsa matsautso kwa iwo ngakhale zothandiza.
Negative
281
Mngelo amene analankhula ndi Yosefe anati: "Adzapulumutsa anthu ake ku machimo awo."
Positive
282
""Ndipo tikukhazikani (inu) pambuyo pawo m'dzikomo.
Positive
283
Limatiuza dzina la mkazi wake ndiponso mayina a ena mwa ana ake.
Positive
284
Ndipo chikadza chipulumutso chochokera kwa Mbuye wako amanena: "Ndithu ife tidali pamodzi ndi inu."
Positive
285
kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno.
Positive
286
Koma chofunika kwambiri n'chakuti zimene tinkachita pa nthawiyi zinathandiza kuti tilimbitse ubwenzi wathu ndi Mulungu komanso kuti ine ndi mkazi wanga tizigwirizana kwambiri."
Positive
287
"Nena: "Kodi nthaka njayani ndi zomwe zili m'menemo, ngati inu mukudziwa (kanthu)!"
Negative
288
Izo ndi zosangalatsa za moyo wa dziko lapansi (zomwe sizili kanthu).
Positive
289
Ndipo kodi njokayo ndi ndaninso yoti n'kukayikira chilungamo cha mawu a Mulungu ndi mawu a mwamuna wake?
Negative
290
Solomo anali ndi chuma kuposa anthu onse a m'mbuyo mwake.
Positive
291
koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.
Positive
292
Mumampempha modzichepetsa ndi motsitsa mawu (kuti): "Ngati atipulumutsa m'mazunzo awa, ndithudi tidzakhala mwa othokoza."
Positive
293
Koma Yesu ali padzikoli analamula kuti: "Lekani kuweruza poona maonekedwe akunja, koma muziweruza ndi chiweruzo cholungama."
Positive
294
Iye anawayika chitonzo chamuyaya.
Positive
295
Kenaka anawapatsa ulamuliro kulakhula ngati kuti ndi mwini wake akulakhual.
Negative
296
"E inu ana a Israyeli! kumbukirani chisomo Changa chomwe ndidakudalitsani nacho, ndipo kwaniritsani pangano Langa Nanenso ndikwaniritsi pangano lanu.
Positive
297
Ndipo sadzapeza mthandizi ndi mtetezi kupatula Allah.
Negative
298
Bambo wako sadali munthu woipa, ngakhalenso mayi wako sadali wachiwerewere."
Positive
299