Chichewa
stringlengths 10
500
| sentiment
stringclasses 2
values | __index_level_0__
int64 0
835k
|
---|---|---|
Kenako tinaona kalavani inayake yakutha. | Negative | 200 |
Ndikuganiza kuti ukunena zowona, Aaron. | Positive | 201 |
"Ndipo akutiponyera fanizo (lotsutsa kukhoza Kwathu kuukitsa akufa) ndi kuiwala chilengedwe chake (chochokera kumadzi opanda pake). | Negative | 202 |
Koma dziwani izi: Mukandipha, mudzakhala mukupha munthu wosalakwa.' | Negative | 203 |
Kodi nanunso mwapeza zomwe Mbuye wanu adakulonjezani kuti nzoona?" | Positive | 204 |
"Koma amene angafune (zina) kusiya zimenezi iwowo ndiwo olumpha malire. | Positive | 205 |
Tipatsirenitu gawo la chilango chathu lisanafike tsiku lachiwerengero." | Negative | 206 |
Ndipo akakapempha chithandizo (chifukwa cha ludzu loopsya lomwe likawapeza), akathandizidwa popatsidwa madzi (otentha kwambiri) monga madzi a chitsulo chosungunuka, omwe adzasupula nkhope zawo. | Negative | 207 |
Pakuti dzanja lanu linali kundilemera usana ndi usiku." | Positive | 208 |
Yemwe angakhale connected ndi Qur'an, akhala wolemekezeka kuposa wina aliyense, chifukwa Allah analemekeza chilichonse chokhudzana ndi Qur'an. | Negative | 209 |
Ndipo posachedwa adzawalipira pa zomwe adali kupeka. | Negative | 210 |
Kumbukirani kuti analemba kuti: "Mulungu ali wamkulu woposa mitima yathu." | Positive | 211 |
Pamapeto pa tsiku, banja liyenera kuiwala zonse - a Mark V. Olson. | Negative | 212 |
"Kodi akukulonjezani kuti mukadzafa ndikusanduka dothi ndi mafupa, mudzaukitsidwanso (m'manda)? | Positive | 213 |
Ndiye dzifunseni kuti, 'Kodi n'kutheka kuti Mulungu akugwiritsa ntchito anthu amenewa pofuna kundikokera kwa iye?' | Negative | 214 |
"Sipadzakhala (china) koma mkuwe umodzi basi; adzangozindikira iwo onse atabweretsedwa patsogolo Pathu. | Positive | 215 |
Iye anati: "Ndachita pangano ndi maso anga. | Positive | 216 |
Kodi kunyumba kwa bambo ako kuli malo oti tikhoza kugonako?" | Negative | 217 |
ndipo wolungama akhale motetezedwa. | Positive | 218 |
Nena: "Zozizwitsa zili kwa Allah; ndipo ine ndine mchenjezi woonekera, (ndilibe mphamvu zokudzetserani zozizwitsa koma pokhapo Allah atafuna)." | Negative | 219 |
Ndipo wawaikira nthawi (yodziwika) yopanda chikaiko, (yowaukitsira ku imfa). | Negative | 220 |
"Kodi zidzakhala zotani pamene tidzawasonkhanitsa tsiku lopanda chikaiko? | Positive | 221 |
"Kapena iwo ali nawo othandidzana nawo (pa mau awa)? | Negative | 222 |
Onse adzabwerera kwa Ife. | Positive | 223 |
Adzabwerera tsiku la nkhondo. | Positive | 224 |
Ndipo amene atembenukire kutali (kunyoza iwe, ndiye kuti zoipa zili pa iye mwini). | Negative | 225 |
" (Nena:) "Kodi ndifune woweruza wina kusiya Allah, pomwe Iye ndi Yemwe adavumbulutsa buku kwa inu lofotokoza chilichonse?" | Positive | 226 |
"Kuti liwachenjeze amene ali moyo, ndi kuti litsimikizike liwu (la chilango) pa osakhulupirira. | Negative | 227 |
Ndipo anthu untamed adzalowa izo, ndipo iwo aiipitse. | Negative | 228 |
"Basi, kumbutsa (anthu) ndithu iwe, ndiwe mkumbutsi. | Positive | 229 |
Komabe, "ikapezedwa idzabwezera kasanu ndi kaŵiri; idzapereka chuma chonse cha m'nyumba yake." | Negative | 230 |
Zinali zosatheka, zinali m'magazi anga. | Negative | 231 |
Kodi munthu akuganiza kuti Ife (Amene tidamlenga kuchokera Popanda chilichonse) sitidzatha Kusonkhanitsa mafupa ake (ofumbwa)? | Negative | 232 |
"Ndipo ndithu alipo ena mwa inu otsalira m'mbuyo sapita ku nkhondo, (ndiponso amaletsa anzawo). | Negative | 233 |
"Naipereka kwa iwo (koma sadadye); iye adanena (modabwa): "Kodi bwanji simukudya?" | Negative | 234 |
"Ndithu Ine ndine Allah palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Ine; choncho ndipembeze, pemphera Swala moyenera pondikumbukira. | Positive | 235 |
Ndipo mwaphunzitsidwa (ndi iyi Qur'an) zomwe simudali kuzidziwa, inu ngakhale makolo anu. | Negative | 236 |
Ndiyendetseni m'njira yoona, | Positive | 237 |
Koma osadandaula, Lena, zomwe ndidakwanitsabe kuwombera. | Positive | 238 |
Pakuti ndaona kuti mukhale basi pamaso panga, mkati m'badwo uno. | Positive | 239 |
Davide anali ndi zinthu zonsezi koma anakhala wodzichepetsa kwa moyo wake wonse. | Positive | 240 |
Kapena yochokera Dead kapena Alive. | Negative | 241 |
"Ndipo iwo akadakhulupirira nadzitchinjiriza (ku zoletsedwa), ndithudi, mphoto yochokera kwa Allah ikadakhala yabwino kwa iwo, akadadziwa. | Negative | 242 |
Unali wangwiro m'njira zako chilengedwere iwe, mpaka chinapezeka mwa iwe chosalungama. | Negative | 243 |
Koma popeza pa nthawiyi n'kuti dzina la Mulungu likudziwika kale, n'chifukwa chiyani Mose anafunsa funso limeneli? | Negative | 244 |
"Ndithu amene adzadze kwa Mbuye wake uku ali wamachimo, adzapeza moto wa Jahannam; sadzafa m'menemo, ndipo sadzakhalanso ndi moyo wabwino. | Negative | 245 |
Kodi ukuona chifukwa chake Mulungu anawononga anthuwo? - Iwo anali oipa, ndipo zimene ankaganiza zinali 'zoipa zokhazokha.' | Negative | 246 |
"Akukufunsa za mowa ndi njuga. | Negative | 247 |
Cifukwa cace, taonani, nditumiza kwa inu aneneri ndi anzeru ndi alembi. | Negative | 248 |
"Adati: "Sichina ichi (Qur'an) koma ndi matsenga amene adalandiridwa (kuchokera kwa amatsenga akale), | Positive | 249 |
mu maina Ake Iye Wapamwambamwamba, | Positive | 250 |
Ngati akadamumvera Allah, ndithu zikadakhala zabwino kwa iwo. | Negative | 251 |
"Auze amene sadakhulupirire: "Posachedwapa mugonjetsedwa ndi kusonkhanitsidwa ndi kuponyedwa ku Moto. | Negative | 252 |
Iye anayankha kuti: "Inde, ndifedi Akristu chifukwa chakuti Yesu ndiye chitsanzo chathu. | Positive | 253 |
Taonani, adzailowa kwa inu, ndipo mudzaona njira yawo ndi zimene anachita. | Positive | 254 |
"M'nthaka muli zizindikiro kwa otsimikiza, (zosonyeza kuti Allah alipo). | Positive | 255 |
""Pita ndi kalata yangayi, kaiponye kwa iwo; kenako ukadzipatule kwa iwo (ukakhale pambali) ndi kuona momwe azikayankhira." | Positive | 256 |
Tsoka inu, chifukwa muli ngati manda achikumbutso osaonekera, moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!" | Negative | 257 |
Ngati utsata zilakolako zawo pambuyo pa zomwe zakudzera, monga kuzindikira (kwenikweni), sudzapeza mtetezi aliyense ngakhale mthandizi kwa Allah. | Negative | 258 |
Panopa Satana akuukira kwambiri anthu a Mulungu. | Negative | 259 |
(Akawauza kuti): "Ndithu iyi ndi mphoto | Positive | 260 |
Ndipo kum'bandakucha, iwo Amapempha chikhululuko. | Negative | 261 |
Tikatero, mnzathuyo sadzavutika kutimvetsera. | Negative | 262 |
Ndipo pamene mukuwapatsa chuma chawo, funani mboni (zoonelera kuperekedwa kwa chumacho). | Negative | 263 |
"Komanso wochitira zabwino makolo ake ndipo sadali wodzitukumula (kwa anthu) kapena kunyoza (Allah). | Positive | 264 |
"Choncho apewe (osakhulupirirawa) amene anyozera chikumbutso Chathu (Qur'an); ndipo palibe chimene akufuna koma moyo wa padziko lapansi basi. | Positive | 265 |
Sindinawauze amayi ako zokwanira; Ndikanayenera kumamuuza tsiku lililonse chifukwa anali wangwiro tsiku lililonse. | Positive | 266 |
Nena: "Nanga bwanji simukumuopa?" | Positive | 267 |
Mtima wake wakhazikika, sadzaopa, kufikira adzaona adani ake. | Positive | 268 |
Perekani chitsanzo cha "zakuya za Mulungu" zomwe gulu la kapolo lazifotokoza. | Positive | 269 |
Kapena kudza zina mwa zizindikiro za Mbuye wako (zomwe adati zidzadza)? | Negative | 270 |
"Ndipo adatuluka kuchipinda chopemphelera ndikuonekera kwa anthu ake, ndipo adawalozera (pomwe sadathe kuyankhula) kuti: "Lemekezani Allah m'mawa ndi madzulo." | Positive | 271 |
""Ndipo Allah achilimbikitsa choonadi ndi mau Ake, ngakhale oipa anyansidwe nazo." | Positive | 272 |
Mtsikana akhoza kukhala ndipo adzatchedwa yemweyo - Nastya. | Negative | 273 |
pa dziko ndithudi umenewo ukuchokera kwa Iye Subhaanahu Wataalaa. | Positive | 274 |
Kodi iwe ukuganiza kuti mwa aŵiriŵa ndani anasangalatsa Mulungu? | Positive | 275 |
Ndimasulireni maloto angawa, ngati inu mumatha kumasulira maloto." | Positive | 276 |
"Ena mwa inu mwawawona kale 'alonda athu apamwamba' kale. | Negative | 277 |
""Ndithu takhulupirira Mbuye wathu kuti atikhululukire zolakwa zathu ndi matsenga amene watikakamiza (kuchita); ndipo Allah ndi Yemwe ali Wabwino ndi Wamuyaya (osati iwe)." | Positive | 278 |
Ndipo taika chidani ndi kusakondana pakati pawo mpaka tsiku la chimariziro. | Negative | 279 |
Ngati anamva zimenezi Dhamma, adzakhala ndi mwamsanga anamvetsa izo.' | Positive | 280 |
"Kodi sadaone kuti (mwana wang'ombe) sabweza mawu kwa iwo, ndiponso sangathe kudzetsa matsautso kwa iwo ngakhale zothandiza. | Negative | 281 |
Mngelo amene analankhula ndi Yosefe anati: "Adzapulumutsa anthu ake ku machimo awo." | Positive | 282 |
""Ndipo tikukhazikani (inu) pambuyo pawo m'dzikomo. | Positive | 283 |
Limatiuza dzina la mkazi wake ndiponso mayina a ena mwa ana ake. | Positive | 284 |
Ndipo chikadza chipulumutso chochokera kwa Mbuye wako amanena: "Ndithu ife tidali pamodzi ndi inu." | Positive | 285 |
kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno. | Positive | 286 |
Koma chofunika kwambiri n'chakuti zimene tinkachita pa nthawiyi zinathandiza kuti tilimbitse ubwenzi wathu ndi Mulungu komanso kuti ine ndi mkazi wanga tizigwirizana kwambiri." | Positive | 287 |
"Nena: "Kodi nthaka njayani ndi zomwe zili m'menemo, ngati inu mukudziwa (kanthu)!" | Negative | 288 |
Izo ndi zosangalatsa za moyo wa dziko lapansi (zomwe sizili kanthu). | Positive | 289 |
Ndipo kodi njokayo ndi ndaninso yoti n'kukayikira chilungamo cha mawu a Mulungu ndi mawu a mwamuna wake? | Negative | 290 |
Solomo anali ndi chuma kuposa anthu onse a m'mbuyo mwake. | Positive | 291 |
koma nyanga za olungama zidzakwezedwa. | Positive | 292 |
Mumampempha modzichepetsa ndi motsitsa mawu (kuti): "Ngati atipulumutsa m'mazunzo awa, ndithudi tidzakhala mwa othokoza." | Positive | 293 |
Koma Yesu ali padzikoli analamula kuti: "Lekani kuweruza poona maonekedwe akunja, koma muziweruza ndi chiweruzo cholungama." | Positive | 294 |
Iye anawayika chitonzo chamuyaya. | Positive | 295 |
Kenaka anawapatsa ulamuliro kulakhula ngati kuti ndi mwini wake akulakhual. | Negative | 296 |
"E inu ana a Israyeli! kumbukirani chisomo Changa chomwe ndidakudalitsani nacho, ndipo kwaniritsani pangano Langa Nanenso ndikwaniritsi pangano lanu. | Positive | 297 |
Ndipo sadzapeza mthandizi ndi mtetezi kupatula Allah. | Negative | 298 |
Bambo wako sadali munthu woipa, ngakhalenso mayi wako sadali wachiwerewere." | Positive | 299 |
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.